26 Ndipo amphamvuwo a magulu a nkhondo ndiwo Asaheli mbale wa Yoabu, Elanani mwana wa Dodo wa ku Betelehemu,
27 Samoti Mharori, Helezi Mpeloni,
28 Ira mwana wa Ikesi wa ku Tekoi, Abiezeri wa ku Anatoti,
29 Sibekai Mhusati, liai M-ahohi,
30 Maharai Mnetofati, Heledi mwana wa Bana Mnetofati,
31 Itai mwana wa Ribai wa Gibeya wa ana a Benjamini, Benaya Mpiratoni,
32 Horai wa ku mitsinje ya Gaasi, Abiyeli M-ariba,