1 Mbiri 11:3 BL92

3 Akuru onse omwe a Israyeli anadza kwa mfumu ku Hebroni; ndipo Davide anapangana nao pangano ku Hebroni pamaso pa Yehova; ndipo anamdzoza Davide akhale mfumu ya Israyeli monga mwa mau a Yehova, ndi lizanja la Samueli.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 11

Onani 1 Mbiri 11:3 nkhani