8 Pamene Afilisti anamva kuti anamdzoza Davide akhale mfumu ya Aisrayeli onse, Afilisti onse anakwera kufunafuna Davide; ndipo Davide anamva, nawaturukira.
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 14
Onani 1 Mbiri 14:8 nkhani