12 Inu ndinu akuru a nyumba za makolo a Alevi, mudzipatule inu ndi abale anu omwe, kuti mukatenge ndi kukwera nalo likasa la Yehova Mulungu wa Israyeli ku malo ndalikonzera.
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 15
Onani 1 Mbiri 15:12 nkhani