1 Mbiri 17:21 BL92

21 Ndiwo ayani akunga anthu anu Israyeli, mtundu wa pa wokha wa pa dziko lapansi, amene Mulungu anakadziombolera mtundu wa anthu, kudzibukitsira dzina, mwa zazikuru ndi zoopsa, pakupitikitsa amitundu pamaso pa anthu anu amene munawaombola m'Aigupto?

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 17

Onani 1 Mbiri 17:21 nkhani