1 Mbiri 18:10 BL92

10 anatumiza Hadoramu mwana wace kwa Davide, kumlankhula ndi kumdalitsa, popeza adayambana ndi Hadarezeri, namkantha; pakuti Hadarezeri adacita nkhondo ndi Tou; ndipo anali nazo zipangizo za mitundu mitundu za golidi ndi siliva ndi mkuwa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 18

Onani 1 Mbiri 18:10 nkhani