1 Mbiri 2:23 BL92

23 Ndi Gesuri ndi Aramu analanda midzi ya Yairi, pamodzi ndi Kenati ndi miraga yace; ndiyo midzi makumi asanu ndi limodzi. Iwo onse ndiwo ana a Makiri atate wa Gileadi.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 2

Onani 1 Mbiri 2:23 nkhani