1 Mbiri 2:42 BL92

42 Ndi ana a Kalebi mbale wa Yerameli ndiwo Mesa mwana wace woyamba, ndiye atate wa Zifi; ndi ana a Maresa atate wa Hebroni.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 2

Onani 1 Mbiri 2:42 nkhani