1 Mbiri 21:26 BL92

26 Ndipo Davide anamangira Yehova guwa la nsembe komweko; napereka nsembe zopsereza, ndi nsembe zoyamika, naitana kwa Yehova; ndipo anamyankha ali m'Mwamba ndi mota pa guwa la nsembe yopsereza.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 21

Onani 1 Mbiri 21:26 nkhani