1 Mbiri 21:29 BL92

29 Pakuti kacisi wa Yehova amene Mose anapanga m'cipululu, ndi guwa la nsembe yopsereza, zinali pa msanje wa ku Gibeoni nthawi yomweyi.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 21

Onani 1 Mbiri 21:29 nkhani