1 Mbiri 23:24 BL92

24 Awa ndi ana a Levi monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo akuru a nyumba za makolo a iwo owerengedwa mwa ciwerengo ca maina mmodzi mmodzi, akugwira nchito ya utumiki wa nyumba ya Yehova, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 23

Onani 1 Mbiri 23:24 nkhani