22 Wa Aizari: Selomoti; wa ana a Selomoti, Yahati.
23 Ndi wa ana a Hebroni: mkuru ndi Yeriya, waciwiri Amariya, wacitatu Yahazieli, wacinai Yekameamu.
24 Wa ana a Uziyeli, Mika; wa ana a Mika, Samiri.
25 Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya,
26 Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.
27 Ana a Merari: wa Yaziya, Beno, ndi Sohamu, ndi Sakuri, ndi Ibri.
28 Wa Mali: Eleazara, ndiye wopanda ana.