24 Wa ana a Uziyeli, Mika; wa ana a Mika, Samiri.
25 Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya,
26 Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.
27 Ana a Merari: wa Yaziya, Beno, ndi Sohamu, ndi Sakuri, ndi Ibri.
28 Wa Mali: Eleazara, ndiye wopanda ana.
29 Wa Kisi: mwana wa Kisi, Yerameli.
30 Ndi ana a Musi: Mali, ndi Ederi, ndi Yerimoti, Awa ndi ana a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao.