7 Ndipo maere oyamba anamgwera Yehoyaribu, waciwiri Yedaya,
8 wacitatu Harimu, wacinai Seorimu,
9 wacisanu Malikiya, wacisanu ndi cimodzi Miyamini,
10 wacisanu ndi ciwiri Hakozi, wacisanu ndi citatu Abiya,
11 wacisanu ndi cinai Yesuwa, wakhumi Sekaniya,
12 wakhumi ndi cimodzi Eliyasibu, wakhumi ndi ciwiri Yakimu,
13 wakhumi ndi citatu Hupa, wakhumi ndi cinai Yesebeabu,