1 Mbiri 26:12 BL92

12 Mwa iwowa munali magawidwe a odikira, mwa akulu a amuna akucita udikiro wao, monga abale ao, kutumikira m'nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 26

Onani 1 Mbiri 26:12 nkhani