16 Koma oyang'anira mafuko a lsrayeli ndi awa: wa Arubeni mtsogoleri wao ndiye Eliezeri mwana wa Zikiri; wa Asimeoni, Sefatiya mwana wa Maaka;
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 27
Onani 1 Mbiri 27:16 nkhani