6 ndi Ibara, ndi Elisama, ndi Elifeleti,
7 ndi Noga, ndi Nefegi, ndi Yafiya,
8 ndi Elisama, ndi Eliada, ndi Elifeleti, asanu ndi anai.
9 Onsewa ndiwo ana a Davide, pamodzi ndi ana a akazi ang'ono; ndipo Tamara ndiye mlongo wao.
10 Ndipo mwana wa Solomo ndiye Rehabiamu, Abiya mwana wace, Asa mwana wace, Yeo hosafati mwana wace,
11 Yoramu mwana wace, Ahaziya mwana wace, Yoasi mwana wace,
12 Amaziya mwana wace, Azariya mwana wace, Yotamu mwana wace,