1 Mbiri 4:18 BL92

18 Ndi mkazi wace Myuda anabala Yeredi atate wa Gedoro, ndi Heberi atate wa Soko, ndi Yekutiyeli atate wa Zanowa. Ndipo awa ndi ana a Bitiya mwana wamkazi wa Farao, amene Meredi anamtenga.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 4

Onani 1 Mbiri 4:18 nkhani