1 Mbiri 6:32 BL92

32 Ndipo anatumikira ndi kuyimba pakhomo pa kacisi wa cihema cokomanako mpaka Solomo adamanga nyumba ya Yehova m'Yerusalemu, naimirira m'utumiki wao monga mwa malongosoledwe ao.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 6

Onani 1 Mbiri 6:32 nkhani