1 Mbiri 6:49 BL92

49 Koma Aroni ndi ana ace adafofukiza pa guwa la nsembe yopsereza, ndi pa guwa la nsembe yofukiza, cifukwa ca nchito yonse ya malo opatulikitsa, ndi kucitira Israyeli cowatetezera, monga mwa zonse Mose mtumiki wa Mulungu adawauza.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 6

Onani 1 Mbiri 6:49 nkhani