22 ndi Isipani, ndi Eberi, ndi Elieli,
23 ndi Abidoni, ndi Zikiri, ndi Hanani,
24 ndi Hananiya, ndi Elamu, ndi Antotiya,
25 ndi Ifideya, ndi Penueli, ana a Sasaki;
26 ndi Samserai, ndi Sehariya, ndi Ataliya,
27 ndi Yaaresiya ndi Eliya, ndi Zikiri, ana a Yerohamu.
28 Awa ndi akuru a nyumba za makolo mwa mibadwo yao, ndiwo akuru anakhala m'Yerusalemu awa.