25 ndi Ifideya, ndi Penueli, ana a Sasaki;
26 ndi Samserai, ndi Sehariya, ndi Ataliya,
27 ndi Yaaresiya ndi Eliya, ndi Zikiri, ana a Yerohamu.
28 Awa ndi akuru a nyumba za makolo mwa mibadwo yao, ndiwo akuru anakhala m'Yerusalemu awa.
29 Ndipo m'Gibeoni anakhala atate a Gibeoni, dzina la mkazi wace ndiye Maaka;
30 ndi mwana wace woyamba ndiye Abidoni, opondana naye ndi Zuri, ndi Kisi, ndi Baala, ndi Nadabu,
31 ndi Gedoro, ndi Ahiyo, ndi Zekeri.