31 ndi Gedoro, ndi Ahiyo, ndi Zekeri.
32 Ndipo Mikiloti anabala Simeya. Ndi iwonso anakhala pamodzi ndi abale ao m'Yerusalemu, popenyana ndi abale ao.
33 Ndipo Neri anabala Kisi, ndi Kisi anabala Sauli, ndi Sauli anabala Yonatani, ndi Malikisuwa, ndi Abinadabu, ndi Esibaala.
34 Ndi mwana wa Yonatani ndiye Meri-baala; ndi Meri-baala anabala Mika.
35 Ndi ana a Mika: Pitoni, ndi Meleki, ndi Tareya, ndi Ahazi.
36 Ndi Ahazi anabala Yehoada, ndi Yehoada anabala Alemeti, ndi Azimaveti, ndi Zimri; ndi Zimri anabala Moza;
37 ndi Moza anabala Bineya, mwana wace ndiye Rafa, mwana wace Eleasa, mwana wace Azeli;