36 ndi mwana wace woyamba ndiye Abidoni, opandana naye ndi Zuri, ndi Kisi, ndi Baala, ndi Neri, ndi Nadabu,
37 ndi Gedoro, ndi Ahiya, ndi Zekariya, ndi Mikiloti.
38 Ndi Mikiloti anabala Simeamu. Ndipo iwonso anakhala pamodzi ndi abale ao m'Yerusalemu, pandunji pa abale ao.
39 Ndipo Neri anabala Kisi, ndi Kisi anabala Sauli, ndi Sauli anabala Yonatani, ndi Malikisuwa, ndi Abinadabu, ndi Esbaala.
40 Ndipo mwana wa Yonatani ndiye Meribaala; ndi Meribaala anabala Mika.
41 Ndi ana a Mika: Pitoni, ndi Meleki, ndi Tareya, ndi Ahazi.
42 Ndi Ahazi anabala Yara, ndi Yara anabala Ameleti, ndi Azmaveti, ndi Zimri; ndi Zimri anabala Moza,