3 Ndipo akuru a ku Yabezi ananena naye, Mutipatse masiku asanu ndi awiri, kuti titumize mithenga m'malire onse a Israyeli; ndipo pakapanda kuoneka wotipulumutsa ife, tidzaturukira kwa inu.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 11
Onani 1 Samueli 11:3 nkhani