14 Mukaopa Yehova ndi kumtumikira ndi kumvera mau ace, ndi kusakana lamulo lace la Yehova, ndipo inu ndi mfumu imene iweruza inu mukadzatsata Yehova Mulungu wanu, cabwino.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 12
Onani 1 Samueli 12:14 nkhani