20 Ndipo Samueli ananena kwa anthuwo, Musaope; munacitadi coipa ici conse, koma musaleka kutsata Yehova, koma mutumikire Yehova ndi mtima wanu wonse;
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 12
Onani 1 Samueli 12:20 nkhani