7 Cifukwa cace tsono, imani pano, kuti ndiweruzane nanu pamaso pa Yehova za nchito zonse zolungama za Yehova, anakucitirani inu ndi makolo anu.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 12
Onani 1 Samueli 12:7 nkhani