7 Ndipo Ahebri ena anaoloka Yordano nafika ku dziko la Gadi ndi Gileadi; koma Sauli akali ku Giligala, ndipo anthu onse anamtsata ndi kunthunthumira.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 13
Onani 1 Samueli 13:7 nkhani