33 Ndipo Samueli anati, Monga lupanga lako linacititsa akazi ufedwa, momwemo mai wako adzakhala mfedwa mwa akazi. Ndipo Samueli anamdula Agagi nthuli nthuli pamaso pa Yehova ku Giligala.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 15
Onani 1 Samueli 15:33 nkhani