35 Ndipo Samueli sanadzanso kudzaona Sauli kufikira tsiku la imfa yace; koma Samueli analira cifukwa ca Sauli; ndipo Yehova anali ndi cisoni kuti anamlonga Sauli mfumu ya Israyeli.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 15
Onani 1 Samueli 15:35 nkhani