1 Samueli 16:12 BL92

12 Ndipo anatumiza munthu, nabwera naye. Tsono iye anali wofiirira, ndi wa nkhope yokongola, ndi maonekedwe okoma. Ndipo Yehova anati, Nyamuka umdzoze, pakuti ndi ameneyu.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 16

Onani 1 Samueli 16:12 nkhani