17 Ndipo Jese anati kwa Davide mwana wace, Uwatengere abale ako efa watirigu uyu wokazinga, ndi mikate iyi khumi, nuthamangire nazo kuzithando kwa abale ako;
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17
Onani 1 Samueli 17:17 nkhani