50 Comweco Davide anapambana Mfilistiyo ndi mwala wa coponyera cace, nakantha Mfilistiyo, namupha. Koma m'dzanja la Davide munalibe lupanga.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17
Onani 1 Samueli 17:50 nkhani