9 Akakhoza iyeyo kuponyana ndi ine ndi kundipha, tidzakhala ife akapolo anu; koma ine ndikamlaka, ndi kumupha, tsono mudzakhala inu akapolo athu, ndi kutitumikira ife.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17
Onani 1 Samueli 17:9 nkhani