1 Samueli 18:10 BL92

10 Ndipo kunali m'mawa mwace, mzimu woipa wocokera kwa Mulungu unamgwira Sauli mwamphamvu, iye nalankhula moyaruka m'nyumba yace; koma Davide anayimba ndi dzanja lace, monga amacita tsiku ndi tsiku; koma m'dzanja la Sauli munali mkondo.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 18

Onani 1 Samueli 18:10 nkhani