21 Nati Sauli, Ndidzampatsa iye, kuti amkhalire msampha, ndi kuti dzanja la Afilisti limgwere. Cifukwa cace Sauli ananena ndi Davide, Lero udzakhala mkamwini wanga kaciwiri.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 18
Onani 1 Samueli 18:21 nkhani