1 Samueli 19:2 BL92

2 Koma Jonatani mwana wa Sauli anakondwera kwambiri ndi Davide. Ndipo Jonatani anauza Davide, nati, Sauli atate wanga alikufuna kukupha; cifukwa cace tsono ucenjere m'mawa, mukhale m'malo mosadziwika, nubisale;

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 19

Onani 1 Samueli 19:2 nkhani