22 Pamenepo iyenso anamuka ku Rama, nafika ku citsime cacikuru ciri ku Seku, nafunsa Dati, Samueli ndi Davide ali kuti? Ndipo wina anati, Taonani, ali ku Nayoti m'Rama.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 19
Onani 1 Samueli 19:22 nkhani