15 Ngakhale asanayambe kupsereza mafuta, amadza mnyamata wa wansembe, namuuza wopereka nsembe, nati, Umpatse wansembeyo nyama yoti akaoce; pakuti safuna nyama yako yophika koma yaiwisi.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 2
Onani 1 Samueli 2:15 nkhani