9 Pamenepo Doegi wa ku Edomu, anaimirira ndi anyamata a Sauli, nayankha, nati, Ine ndinamuona mwana wa Jeseyo alikufika ku Nobi, kwa Ahimeleki mwana wa Ahitubu.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 22
Onani 1 Samueli 22:9 nkhani