11 Kodi ndidzatenga mkate wanga, ndi madzi anga, ndi nyama imene ndinaphera osenga nkhosa anga, ndi kuzipatsa anthu amene sindidziwa kumene afumira?
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25
Onani 1 Samueli 25:11 nkhani