24 Ndipo atagwadira pa mapazi ace anati, Pa ine, mbuye wanga, pa ine pakhale ucimowo; ndipo mulole mdzakazi wanu alankhule m'makutu anu, nimumvere mau a mdzakazi wanu.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25
Onani 1 Samueli 25:24 nkhani