1 Samueli 25:25 BL92

25 Mbuye wanga, musasamalire munthu uyu woipa, ndiye Nabala; cifukwa monga dzina lace momwemo iye; dzina lace ndiye Nabala, ndipo ali nako kupusa; koma ine mdzakazi wanu sindinaona anyamata a mbuye wanga, amene munawatumiza.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25

Onani 1 Samueli 25:25 nkhani