1 Samueli 25:34 BL92

34 Pakuti ndithu, Pali Yehova Mulungu wa Israyeli, amene anandiletsa lero kusapweteka iwe, ukadapanda kufulumira kubwera kundicingamira, zoonadi sindikadasiyira Nabala kufikira kutaca kanthu konse, ngakhale mwana wamwamunammodzi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25

Onani 1 Samueli 25:34 nkhani