1 Samueli 26:12 BL92

12 Comweco Davide anatenga mkondowo, ndi cikho ca madzi ku mutu wa Sauli nacoka iwowa, osawaona munthu, kapena kuzidziwa, kapena kugalamuka; pakuti onse anati m'tulo; popeza tulo tatikuru tocokera kwa Yehova tinawagwira onse.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 26

Onani 1 Samueli 26:12 nkhani