20 Pomwepo Sauli anagwa pansi tantha, naopa kwakukuru, cifukwa ca mau a Samueli; ndipo analibe mphamvu; pakuti tsiku lonse ndi usiku wace wonse anakhala osadya kanthu.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 28
Onani 1 Samueli 28:20 nkhani