1 Samueli 28:4 BL92

4 Ndipo Afilisti anasonkhana, nadza namanga misasa ku Sunemu; ndipo Sauli anasonkhanitsa Aisrayeli onse, namanga iwo ku Giliboa.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 28

Onani 1 Samueli 28:4 nkhani