1 Ndipo mwanayo Samueli anatumikira Yehova pamaso pa Eli. Ndipo masiku aja mau a Yehova anamveka kamodzi kamodzi; masomphenya sanaoneka-oneka.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 3
Onani 1 Samueli 3:1 nkhani