1 Samueli 30:24 BL92

24 Ndipo ndani adzabvomerezana nanu mrandu uwu? Pakuti monga gawo lace la iye wakumuka kunkhondoko, momwemo lidzakhala gawo lace la iye wakukhala ndi akatundu, adzagawana cimodzimodzi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 30

Onani 1 Samueli 30:24 nkhani